Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:66 - Buku Lopatulika

66 Msonkhano wonse pamodzi ndiwo zikwi makumi anai ndi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi asanu ndi limodzi,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

66 Msonkhano wonse pamodzi ndiwo zikwi makumi anai ndi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi asanu ndi limodzi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

66 Chiŵerengero cha anthu onse obwerako ku ukapolo aja chinali 42,360.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:66
3 Mawu Ofanana  

Msonkhano wonse pamodzi ndiwo wa zikwi makumi anai ndi awiri mphambu mazana atatu kudza makumi asanu ndi limodzi,


Ndipo kazembe anawauza kuti asadyeko zopatulika kwambiri, mpaka wauka wansembe wokhala ndi Urimu ndi Tumimu.


osawerenga akapolo ao aamuna ndi aakazi, ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana atatu ndi makumi atatu kudza asanu ndi awiri; ndipo anakhala nao aamuna ndi aakazi oimbira mazana awiri mphambu makumi anai kudza asanu ndi mmodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa