Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:38 - Buku Lopatulika

38 Ana a Senaa, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi anai kudza makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ana a Senaa, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi anai kudza makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 A ku Senaya 3,930.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Zidzukulu za Senaya 3,930.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:38
4 Mawu Ofanana  

Ana a Senaa, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.


Ndi Chipata cha Nsomba anachimanga ana a Hasena; anamanga mitanda yake, ndi kuika zitseko zake, zokowera zake, ndi mipingiridzo yake.


Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza mmodzi.


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa