Nehemiya 5:4 - Buku Lopatulika4 Panali enanso akuti, Takongola ndalama za msonkho wa mfumu; taperekapo chikole minda yathu, ndi minda yathu yampesa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Panali enanso akuti, Takongola ndalama za msonkho wa mfumu; taperekapo chikole minda yathu, ndi minda yathu yampesa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Panali enanso amene ankati, “Ife tachita kukongola ndalama kuti tikhome msonkho wa minda yathu kwa mfumu, ndiponso kuti tikhomere mitengo yathu yamphesa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Panalinso ena amene ankanena kuti, “ife tinachita kukongola ndalama zoti tipereke msonkho wa minda ndi mitengo yathu ya mphesa kwa mfumu. Onani mutuwo |