Nehemiya 5:2 - Buku Lopatulika2 Popeza panali ena akuti, Ife, ana athu aamuna ndi aakazi, ndife ambiri; talandira tirigu, kuti tidye tikhale ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Popeza panali ena akuti, Ife, ana athu aamuna ndi aakazi, ndife ambiri; talandira tirigu, kuti tidye tikhale ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pakuti panali ena amene ankati, “Ife ndi ana athu tikuchuluka kwambiri, motero tikusoŵa tirigu wakudya, kuti tikhale ndi moyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ena ankanena kuti, “Ife ndi ana athu aamuna ndi aakazi, tilipo ochuluka kwambiri. Choncho tikufuna tirigu kuti tidye ndi kukhala ndi moyo.” Onani mutuwo |