Nehemiya 5:19 - Buku Lopatulika19 Mundikumbukire Mulungu, zindikomere zonse ndinachitira anthu awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mundikumbukire Mulungu, zindikomere zonse ndinachitira anthu awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Kuti tipeze bwino, kumbukirani, Inu Mulungu wanga, zonse zimene ndidaŵachitira anthuzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kuti zinthu zindiyendere bwino, kumbukirani Yehova Mulungu wanga pa zonse zimene ndachitira anthu awa. Onani mutuwo |