Nehemiya 5:10 - Buku Lopatulika10 Kodi ine, ndi abale anga, ndi anyamata anga, tiwakongoletsa ndalama ndi tirigu mwa phindu? Ndikupemphani, tileke phindu ili. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kodi ine, ndi abale anga, ndi anyamata anga, tiwakongoletsa ndalama ndi tirigu mwa phindu? Ndikupemphani, tileke phindu ili. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chinanso nchakuti ine, pamodzi ndi abale anga ndiponso antchito anga, tidaŵakongoza ndalama ndi tirigu. Tiyeni tisaŵaumirize kubwezera ngongolezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ine ndi abale anga ndiponso antchito anga tikuwakongozanso anthuwa ndalama ndi tirigu. Ndipo tiyeni tilekeretu zolandira chiwongoladzanja! Onani mutuwo |