Nehemiya 4:8 - Buku Lopatulika8 napangana chiwembu iwo onse pamodzi, kudzathira nkhondo ku Yerusalemu, ndi kuchita chisokonezo m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 napangana chiwembu iwo onse pamodzi, kudzathira nkhondo ku Yerusalemu, ndi kuchita chisokonezo m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono adapangana za chiwembu choti akathire nkhondo Yerusalemu ndi kusokoneza anthu amumzindamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsono onse anapangana za chiwembu kuti abwere ndi kudzathira nkhondo anthu a ku Yerusalemu ndi kuyambitsa mapokoso pakati pawo. Onani mutuwo |