Nehemiya 4:9 - Buku Lopatulika9 Koma tinapemphera kwa Mulungu wathu, ndi kuwaikira olindirira usana ndi usiku, chifukwa cha iwowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma tinapemphera kwa Mulungu wathu, ndi kuwaikira olindirira usana ndi usiku, chifukwa cha iwowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo ife tidapemphera kwa Mulungu wathu, ndipo tidaika alonda oti azititeteza kwa adani athuwo usana ndi usiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma ife tinapemphera kwa Mulungu wathu ndipo tinayika alonda otiteteza kwa adaniwo usiku ndi usana. Onani mutuwo |