Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 4:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo ndinati kwa aufulu, ndi olamulira, ndi anthu otsala, Ntchito ndiyo yochuluka ndi yachitando, ndi ife tili palakepalake palingapo, yense atalikizana ndi mnzake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo ndinati kwa aufulu, ndi olamulira, ndi anthu otsala, Ntchito ndiyo yochuluka ndi yachitando, ndi ife tili palakepalake palingapo, yense atalikizana ndi mnzake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ndidaŵauza atsogoleri ndi akuluakulu ndiponso anthu ena onse aja kuti, “Ntchitoyi njaikulu, ili pa dera lalikulu, ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ndipo ine ndinati kwa anthu olemekezeka ndi anthu ena onse, “Ntchitoyi ndi yayikulu ndipo ili padera lalikulu ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 4:19
2 Mawu Ofanana  

ndi omanga linga aliyense anamangirira lupanga lake m'chuuno mwake, nagwira ntchito motero. Ndipo woomba lipenga anali ndi ine.


paliponse mukumva mau a lipenga, musonkhanire komweko kwa ife; Mulungu wathu adzatigwirira nkhondo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa