Nehemiya 3:28 - Buku Lopatulika28 Kumtunda kwa Chipata cha Akavalo anakonza ansembe, yense pandunji pa nyumba yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Kumtunda kwa chipata cha akavalo anakonza ansembe, yense pandunji pa nyumba yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Kuyambira ku Chipata cha Akavalo, ansembe ena ankakonza khoma, aliyense moyang'anana ndi nyumba yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Kuyambira ku Chipata cha Akavalo anakonza ndi ansembe ena ndipo aliyense amakonza khoma loyangʼanana ndi nyumba yake. Onani mutuwo |