Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 3:29 - Buku Lopatulika

29 Potsatizana nao anakonza Zadoki mwana wa Imeri pandunji pa nyumba yake. Ndi potsatizana naye anakonza Semaya mwana wa Sekaniya, wosunga Chipata cha Kum'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Potsatizana nao anakonza Zadoki mwana wa Imeri pandunji pa nyumba yake. Ndi potsatizana naye anakonza Semaya mwana wa Sekaniya, wosunga chipata cha kum'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Pambali pa iwowo Zadoki, mwana wa Imeri, adakonza chigawo china choyang'anananso ndi nyumba yake. Pambali pa iyeyo Semaya, mwana wa Sekaniya, amene ankasunga Chipata chakuvuma, adakonza chigawo china.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Motsatana nawo, Zadoki mwana wa Imeri anakonza chigawo china choyangʼanana ndi nyumba yake. Motsatana naye, Semeya mwana wa Sekaniya, mlonda wa Chipata cha Kummawa, anakonzanso khoma.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 3:29
8 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Hananiya: Pelatiya, ndi Yesaya, ana a Refaya, ana a Arinani, ana a Obadiya, ana a Sekaniya.


Pamenepo Sekaniya mwana wa Yehiyele, mwana wina wa Elamu, anambwezera Ezara mau, nati, Talakwira Mulungu wathu, tadzitengera akazi achilendo a mitundu ya dzikoli; koma tsopano chimtsalira Israele chiyembekezo kunena za chinthu ichi.


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.


Kumtunda kwa Chipata cha Akavalo anakonza ansembe, yense pandunji pa nyumba yake.


Potsatizana naye Hananiya mwana wa Selemiya, ndi Hanuni mwana wachisanu ndi chimodzi wa Zalafi, anakonza gawo lina. Potsatizana naye anakonza Mesulamu mwana wa Berekiya pandunji pa chipinda chake.


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


nutulukire kuchigwa cha mwana wake wa Hinomu, chimene chili pa khomo la Chipata cha Mapale, nulalikire kumeneko mau amene ndidzakuuza iwe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa