Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 3:27 - Buku Lopatulika

27 Potsatizana nao Atekowa anakonza gawo lina, pandunji pa nsanja yaikulu yosomphoka ndi kulinga la Ofele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Potsatizana nao Atekowa anakonza gawo lina, pandunji pa nsanja yaikulu yosomphoka ndi kulinga la Ofele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Pambali pa Pedaya ndi anzake, Atekowa adakonza chigawo china choyang'anana ndi nsanja ija yaikulu ndi yaitali mpaka kukafika ku khoma la Ofele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Motsatana nawo, anthu a ku Tekowa anakonzanso chigawo china choyangʼanana ndi nsanja ija yayikulu ndi yayitali mpaka ku khoma la Ofeli.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 3:27
2 Mawu Ofanana  

Ndipo panali ngati mapewa anai pansi pangodya zinali za phaka limodzi, mapewawo anali a phaka lomwelo.


Ndi pambali pao anakonza Atekowa; koma omveka ao sanapereke makosi ao kuntchito ya Mbuye wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa