Nehemiya 3:2 - Buku Lopatulika2 Ndi pambali pake anamanga amuna a ku Yeriko. Ndi pambali pao anamanga Zakuri mwana wa Imuri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndi pambali pake anamanga amuna a ku Yeriko. Ndi pambali pao anamanga Zakuri mwana wa Imuri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu a ku Yeriko adamanga chigawo china pambalipa, ndipo Zakuri, mwana wa Imuri, adamanga chigawo chinanso kuyandikana ndi chimenechi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anthu a ku Yeriko anamanga chigawo china pambali pake ndipo Zakuri mwana wa Imuri anamanga chigawo chinanso choyandikana nawo. Onani mutuwo |