Nehemiya 13:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ndinaipidwa nacho kwambiri, motero ndinataya kubwalo akatundu onse a m'nyumba ya Tobiya, kuwachotsa m'chipindamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ndinaipidwa nacho kwambiri, motero ndinataya kubwalo akatundu onse a m'nyumba ya Tobiya, kuwachotsa m'chipindamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pamenepo ndidapsa mtima kwambiri, ndipo ndidamtaya kunja katundu yense wa Tobiya amene anali m'chipindamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndinapsa mtima kwambiri ndipo ndinataya kunja katundu yense wa Tobiya amene anali mʼchipindamo. Onani mutuwo |