Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 13:9 - Buku Lopatulika

9 Pamenepo ndinalamulira, ndipo anayeretsa zipindazo; ndipo ndinabwezeramonso zipangizo za nyumba ya Mulungu, pamodzi ndi zopereka za ufa ndi lubani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pamenepo ndinalamulira, ndipo anayeretsa zipindazo; ndipo ndinabwezeramonso zipangizo za nyumba ya Mulungu, pamodzi ndi zopereka za ufa ndi lubani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsono ndidalamula kuti ayeretse zipindazo. Kenaka ndidabwezeranso ziŵiya za m'Nyumba ya Mulungu, pamodzi ndi zopereka za chakudya ndi lubani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ndinalamulira kuti ayeretse zipinda, ndipo kenaka ndinabwezeramo zida za mʼNyumba ya Mulungu, pamodzi ndi chopereka cha zakudya ndi lubani.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 13:9
5 Mawu Ofanana  

nanena nao, Ndimvereni, Alevi inu, dzipatuleni, nimupatule nyumba ya Yehova Mulungu wa makolo anu, ndi kuchotsa zoipsa m'malo opatulika.


ndi kuti tidzabwera nazo za mtanda wa mkate wathu woyamba, ndi nsembe zathu zokwera, ndi zipatso za mtengo uliwonse, vinyo, ndi mafuta, kwa ansembe, kuzipinda za nyumba ya Mulungu wathu; ndi limodzi la magawo khumi la nthaka yathu kwa Alevi; pakuti Alevi amene amalandira limodzilimodzi la magawo khumi m'midzi yonse yolima ife.


Ndipo iwo anasunga udikiro wa Mulungu wao, ndi udikiro wa mayeretsedwe; momwemonso oimbira ndi odikira, monga mwa lamulo la Davide ndi la Solomoni mwana wake.


Ndipo pa nsanamira za pazipata panali kanyumba ndi chitseko chake; pamenepo anatsuka nsembe yopsereza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa