Nehemiya 13:29 - Buku Lopatulika29 Muwakumbukire Mulungu wanga, popeza anadetsa unsembe, ndi pangano la unsembe, ndi la Alevi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Muwakumbukire Mulungu wanga, popeza anadetsa unsembe, ndi pangano la unsembe, ndi la Alevi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Inu Mulungu wanga, mukumbukire m'mene anthuwo adaipitsira unsembe wao ndi m'mene adanyozera chipangano chimene mudachita ndi Alevi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Inu Mulungu wanga, mukumbukire mmene iwo anayipitsira unsembe, pangano la unsembe komanso la Alevi. Onani mutuwo |