Nehemiya 13:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo kodi tidzamvera inu, kuchita choipa ichi chachikulu chonse, kulakwira Mulungu wathu ndi kudzitengera akazi achilendo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo kodi tidzamvera inu, kuchita choipa ichi chachikulu chonse, kulakwira Mulungu wathu ndi kudzitengera akazi achilendo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Monga tsopano tizimva kuti inunso mumachita choipa chachikulu chomwechi cha kuipira Mulungu pomakwatira akazi achilendo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Kodi tsopano ife tizimva inu kuti mukuchita choyipa chachikulu chimenechi, kupandukira Yehova Mulungu wathu pomakwatira akazi achilendo?” Onani mutuwo |