Nehemiya 13:14 - Buku Lopatulika14 Mundikumbukire Mulungu wanga mwa ichi, nimusafafanize zokoma zanga ndinazichitira nyumba ya Mulungu wanga, ndi maudikiro ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mundikumbukire Mulungu wanga mwa ichi, nimusafafanize zokoma zanga ndinazichitira nyumba ya Mulungu wanga, ndi maudikiro ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inu Mulungu wanga, mundikumbukire ine pa zimenezi. Musaiŵale ntchito zanga zabwino zimene ndachitira Nyumba ya Mulungu wanga pofuna kumtumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Inu Mulungu wanga, mundikumbukire pa zimenezi, ndipo musafafanize ntchito zanga zimene ndachita mokhulupirika pa Nyumba yanu pofuna kukutumikirani. Onani mutuwo |