Nehemiya 13:12 - Buku Lopatulika12 Ndi Ayuda onse anabwera nalo limodzilimodzi la magawo khumi a tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta, kunyumba za chuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi Ayuda onse anabwera nalo limodzilimodzi la magawo khumi a tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta, kunyumba za chuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nditachita zimenezi, Ayuda adayambanso kubwera ndi zopereka za chachikhumi cha tirigu, vinyo ndi mafuta, kuti azipereka ku nyumba zosungira chuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pambuyo pake Ayuda anayambanso kubwera ndi zopereka zawo za chakhumi cha tirigu, vinyo ndi mafuta kuti ziperekedwe ku nyumba yosungiramo chuma. Onani mutuwo |