Nehemiya 13:1 - Buku Lopatulika1 Tsiku lomwelo anawerenga m'buku la Mose m'makutu a anthu, napeza m'menemo kuti Aamoni ndi Amowabu asalowe mu msonkhano wa Mulungu kunthawi yonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tsiku lomwelo anawerenga m'buku la Mose m'makutu a anthu, napeza m'menemo kuti Aamoni ndi Amowabu asalowe mu msonkhano wa Mulungu kunthawi yonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa tsiku limenelo adaŵerenga buku la Mose, anthu onse alikumva. Ndipo adafika pa mau akuti, “Mwamoni kapena Mmowabu asaloŵe konse mu msonkhano wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pa tsiku limenelo anawerenga buku la Mose anthu akumva. Ndipo anapeza mawu akuti, Mwamoni kapena Mmowabu asalowe konse mu msonkhano wa Mulungu. Onani mutuwo |