Nehemiya 12:23 - Buku Lopatulika23 Ana a Levi, akulu a nyumba za makolo, analembedwa m'buku la machitidwe, mpaka masiku a Yohanani mwana wa Eliyasibu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ana a Levi, akulu a nyumba za makolo, analembedwa m'buku la machitidwe, mpaka masiku a Yohanani mwana wa Eliyasibu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adzukulu a Levi, makamaka atsogoleri a mabanja ao, adalembedwa m'buku la Mbiri, mpaka pa nthaŵi ya Yohanani mwana wa Eliyasibu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Zidzukulu za Levi, makamaka atsogoleri a mabanja awo analembedwa mʼbuku la mbiri mpaka pa nthawi ya Yohanani mwana wa Eliyasibu. Onani mutuwo |