Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Nehemiya 12:22 - Buku Lopatulika

22 M'masiku a Eliyasibu, Yoyada, Yohanani, ndi Yaduwa, Alevi analembedwa akulu a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariusi wa ku Persiya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 M'masiku a Eliyasibu, Yoyada, Yohanani, ndi Yaduwa, Alevi analembedwa akulu a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariusi wa ku Persiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Pa nthaŵi ya Eliyasibu, Yoyada, Yohanani ndi Yaduwa, amene anali akulu a ansembe, padalembedwa maina a atsogoleri a mabanja a Alevi ndi a ansembe, mpaka pa nthaŵi imene mfumu Dariusi wa ku Persiya ankalamulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pa nthawi ya Eliyasibu, Yoyada, Yohanani ndi Yaduwa panalembedwa atsogolera a mabanja a Alevi ndi a ansembe mpaka pa nthawi ya ulamuliro wa Dariyo Mperisi.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 12:22
3 Mawu Ofanana  

wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netanele.


Ana a Levi, akulu a nyumba za makolo, analembedwa m'buku la machitidwe, mpaka masiku a Yohanani mwana wa Eliyasibu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa