Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 12:12 - Buku Lopatulika

12 Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe aakulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe aakulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Pa nthaŵi ya Yoyakimu, mkulu wa ansembe, atsogoleri a mabanja a ansembe anali aŵa: Mtsogoleri wa fuko la Seraya anali Meraya. Wa fuko la Yeremiya, anali Hananiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Pa nthawi ya Yowakimu, awa ndiwo anali atsogoleri a mabanja a ansembe: Mtsogoleri wa fuko la Seraya anali Meraya; wa fuko la Yeremiya anali Hananiya;

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 12:12
7 Mawu Ofanana  

Inu ndinu akulu a nyumba za makolo a Alevi, mudzipatule inu ndi abale anu omwe, kuti mukatenge ndi kukwera nalo likasa la Yehova Mulungu wa Israele ku malo ndalikonzera.


Ndipo anapeza kuti amuna aakulu a ana a Eleazara anachuluka, a ana a Itamara anachepa; nawagawa motero: pa ana a Eleazara panali khumi mphambu asanu ndi mmodzi, akulu a nyumba za makolo; ndi pa ana a Itamara, monga mwa nyumba za makolo ao, panali asanu ndi atatu.


ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.


wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanani;


M'masiku a Eliyasibu, Yoyada, Yohanani, ndi Yaduwa, Alevi analembedwa akulu a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariusi wa ku Persiya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa