Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 11:9 - Buku Lopatulika

9 Ndi Yowele mwana wa Zikiri ndiye woyang'anira wao, ndi Yuda mwana wa Hasenuwa ndiye wothandizana naye, poyang'anira mzinda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndi Yowele mwana wa Zikiri ndiye woyang'anira wao, ndi Yuda mwana wa Hasenuwa ndiye wothandizana naye, poyang'anira mudzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Yowele, mwana wa Zikiri, ndiye amene anali kapitao wao. Ndipo Yuda mwana wa Hasenuwa anali kapitao wachiŵiri wa mumzindamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yoweli mwana wa Zikiri ndiye anali mtsogoleri wawo, ndipo Yuda mwana wa Hasenuya ndiye amayangʼanira chigawo cha chiwiri cha mzinda.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 11:9
5 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Benjamini: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Hodaviya, mwana wa Hasenuwa;


Mwa ansembe: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,


Ndipo woyang'anira wa Alevi mu Yerusalemu ndiye Uzi mwana wa Bani, mwana wa Hasabiya, mwana wa Mataniya, mwana wa Mika; mwa ana a Asafu oimbira ena anayang'anira ntchito ya m'nyumba ya Mulungu.


Ndi wotsatana naye Gabai, Salai, mazana asanu ndi anai mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Ndi ana aamuna a Izihara ndiwo: Kora ndi Nefegi, ndi Zikiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa