Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 11:10 - Buku Lopatulika

10 Mwa ansembe: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Mwa ansembe: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ansembe anali aŵa: Yedaya mwana wa Yoyaribu, Yakini,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ansembe anali awa: Yedaya mwana wa Yowaribu; Yakini;

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 11:10
9 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Simeoni: Yemuwele ndi Yamini, ndi Ohadi, ndi Yakini, ndi Zohari, ndi Shaulo, mwana wamwamuna wa mkazi wa ku Kanani.


Ndi a ansembe: Yedaya, ndi Yehoyaribu, ndi Yakini,


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Pamenepo ndinatumiza munthu kuitana Eliyezere, Ariyele, Semaya, ndi Elinatani, ndi Yaribu, ndi Elinatani, ndi Natani, ndi Zekariya, ndi Mesulamu, ndiwo akulu; ndi Yoyaribu ndi Elinatani, ndiwo aphunzitsi.


Seraya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Meraiyoti, mwana wa Ahitubi mtsogoleri wa m'nyumba ya Mulungu;


Ndi Yowele mwana wa Zikiri ndiye woyang'anira wao, ndi Yuda mwana wa Hasenuwa ndiye wothandizana naye, poyang'anira mzinda.


ndi wa Yoyaribu, Matenai; wa Yedaya, Uzi;


Semaya, ndi Yoyaribu, Yedaya.


Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa