Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 11:20 - Buku Lopatulika

20 Ndi Aisraele otsala ndiwo ansembe ndi Alevi, anakhala m'midzi yonse ya Yuda, yense m'cholowa chake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndi Aisraele otsala ndiwo ansembe ndi Alevi, anakhala m'midzi yonse ya Yuda, yense m'cholowa chake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Aisraele ena ndiponso ansembe ndi Alevi otsala anali m'midzi ya Yuda ndipo aliyense ankakhala m'dera la choloŵa chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Aisraeli ena onse pamodzi ndi ansembe ndi Alevi ankakhala mʼmizinda ya Yuda, ndipo aliyense ankakhala mʼdera la makolo ake.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 11:20
3 Mawu Ofanana  

Ndi odikira: Akubu, Talimoni, ndi abale ao akulindira pazipata, ndiwo zana limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.


Awa tsono ndi akulu a dziko okhala mu Yerusalemu; koma m'midzi ya Yuda yense anakhala pa cholowa chake m'midzi mwao, ndiwo Israele, ansembe, ndi Alevi, ndi antchito a m'kachisi, ndi ana a akapolo a Solomoni.


Pamenepo Yoswa anauza anthu amuke, yense ku cholowa chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa