Nehemiya 11:16 - Buku Lopatulika16 ndi Sabetai, ndi Yozabadi, mwa akulu a Alevi, anayang'anira ntchito za pabwalo za nyumba ya Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 ndi Sabetai, ndi Yozabadi, mwa akulu a Alevi, anayang'anira ntchito za pabwalo za nyumba ya Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Sabetai ndiponso Yozabadi anali atsogoleri a Alevi amene ankayang'anira ntchito ya kunja kwa Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Sabetayi ndi Yozabadi anali atsogoleri amene ankayangʼanira ntchito ya kunja kwa Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |