Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 10:8 - Buku Lopatulika

8 Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Maziya, Biligai ndi Semaya. Ameneŵa ndiwo anali ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 10:8
7 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Harimu: Maaseiya, ndi Eliya, ndi Semaya, ndi Yehiyele, ndi Uziya.


Mesulamu, Abiya, Miyamini,


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa ana a Henadadi, Kadimiyele;


wa Biliga, Samuwa; wa Semaya, Yehonatani;


ndi Maaseiya, ndi Semaya, ndi Eleazara, ndi Uzi, ndi Yehohanani, ndi Malikiya, ndi Elamu, ndi Ezere. Ndipo oimbira anaimbitsa Yezeraya ndiye woyang'anira wao.


Potsatizana nao anakonza Zadoki mwana wa Imeri pandunji pa nyumba yake. Ndi potsatizana naye anakonza Semaya mwana wa Sekaniya, wosunga Chipata cha Kum'mawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa