Nehemiya 1:8 - Buku Lopatulika8 Mukumbukire mau mudalamulira mtumiki wanu Mose, ndi kuti, Mukalakwa, ndidzakubalalitsani mwa mitundu ya anthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mukumbukire mau mudalamulira mtumiki wanu Mose, ndi kuti, Mukalakwa, ndidzakubalalitsani mwa mitundu ya anthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kumbukirani mau amene mudauza Mose mtumiki wanu akuti, ‘Ngati mukhala osakhulupirika, ndidzakumwazani pakati pa anthu a mitundu ina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Kumbukirani mawu amene munawuza mtumiki wanu Mose akuti, ‘Ngati mukhala osakhulupirika, ndidzakubalalitsani pakati pa mitundu ina. Onani mutuwo |