Nehemiya 1:7 - Buku Lopatulika7 Tachita mwamphulupulu pa Inu, osasunga malamulo, kapena malemba, kapena maweruzo, amene mudalamulira mtumiki wanu Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tachita mwamphulupulu pa Inu, osasunga malamulo, kapena malemba, kapena maweruzo, amene mudalamulira mtumiki wanu Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tidakuchitirani zoipa zambiri, ndipo sitidamvere mau anu, malamulo anu ndiponso malangizo amene mudapatsa Mose mtumiki wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ife tinakuchitirani zoyipa zambiri. Sitinamvere mawu anu, malamulo ndi malangizo anu amene munapereka kwa mtumiki wanu Mose. Onani mutuwo |