Nehemiya 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo awa ndi akapolo anu ndi anthu anu, amene munawaombola ndi mphamvu yanu yaikulu, ndi dzanja lanu lolimba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo awa ndi akapolo anu ndi anthu anu, amene munawaombola ndi mphamvu yanu yaikulu, ndi dzanja lanu lolimba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Iwoŵa ndiwo atumiki anu ndi anthu anu amene mudaŵapulumutsa ndi mphamvu yanu yaikulu ndi dzanja lanu lolimba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Iwo ndi atumiki anu ndi anthu anu, amene munawawombola ndi mphamvu yanu yayikulu ndi dzanja lanu lamphamvu. Onani mutuwo |