Mlaliki 9:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti amoyo adziwa kuti tidzafa; koma akufa sadziwa kanthu bii, sadzalandira mphotho; pakuti angoiwalika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti amoyo adziwa kuti tidzafa; koma akufa sadziwa kanthu bii, sadzalandira mphotho; pakuti angoiwalika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Amoyo amadziŵa kuti adzafa, koma akufa sadziŵa kanthu, ndipo alibe mphotho inanso yoonjezera. Palibe ndi mmodzi yemwe woŵakumbukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa, koma akufa sadziwa kanthu; alibe mphotho ina yowonjezera, ndipo palibe amene amawakumbukira. Onani mutuwo |