Mlaliki 9:3 - Buku Lopatulika3 Ichi ndi choipa m'zonse zichitidwa pansi pano, chakuti kanthu kamodzi kagwera onse; indetu, mtimanso wa ana a anthu wadzala udyo, ndipo misala ili m'mtima wao akali ndi moyo, ndi pamenepo apita kwa akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ichi ndi choipa m'zonse zichitidwa pansi pano, chakuti kanthu kamodzi kagwera onse; indetu, mtimanso wa ana a anthu wadzala udyo, ndipo misala ili m'mtima wao akali ndi moyo, ndi pamenepo apita kwa akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chimene chili choipa kwambiri mwa zonse zochitika pansi pano ndi ichi chakuti tsoka limodzimodzi limagwera onse. Chinanso nchakuti mitima ya anthu njodzaza ndi zoipa. M'mitima mwao mumadzaza ndi zamisala pamene ali moyo, pambuyo pake kwao nkufa ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Choyipa chimene chili mʼzonse zochitika pansi ndi ichi: Mathero a zonse ndi amodzi. Ndithu, mitima ya anthu ndi yodzaza ndi zoyipa, ndipo mʼmitima mwawo muli zamisala pamene ali ndi moyo, potsiriza pake iwo amakakhala pamodzi ndi anthu akufa. Onani mutuwo |