Mlaliki 8:8 - Buku Lopatulika8 Kulibe munthu ali ndi mphamvu yolamulira mzimu ndi yakutsekereza mzimu; ngakhale mphamvu tsiku la imfa; munkhondo umo mulibe kumasuka; udyo sudzapulumutsa akuzolowerana nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Kulibe munthu ali ndi mphamvu yolamulira mzimu ndi yakutsekereza mzimu; ngakhale mphamvu tsiku la imfa; munkhondo umo mulibe kumasuka; udyo sudzapulumutsa akuzolowerana nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Monga munthu alibe mphamvu zolamulira mpweya wa moyo, chonchonso alibe mphamvu zolamulira tsiku la kufa kwake. Nkhondo sithaŵika, tsono anthu ochita zoipa, kuipa kwaoko sikudzaŵapulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Palibe munthu amene ali ndi mphamvu yolamulira mpweya wa moyo kuti athe kuwusunga, choncho palibe amene ali ndi mphamvu pa tsiku la imfa yake. Nkhondo sithawika; tsono anthu ochita zoyipa, kuyipa kwawoko sikudzawapulumutsa. Onani mutuwo |