Mlaliki 8:7 - Buku Lopatulika7 pakuti sadziwa chimene chidzakhala; pakuti ndani angamuuze nthawi yakuti chidzachitidwa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 pakuti sadziwa chimene chidzakhala; pakuti ndani angamuuze nthawi yakuti chidzachitidwa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Palibe amene amadziŵa zimene zilikudza. Palibe amene angafotokozere zakutsogolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Popeza palibe munthu amene amadziwa zamʼtsogolo, ndani angamuwuze zomwe zidzachitika mʼtsogolo? Onani mutuwo |