Mlaliki 8:6 - Buku Lopatulika6 pakuti kanthu kalikonse kali ndi nthawi yake ndi chiweruzo chake; popeza zoipa za munthu zimchulukira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 pakuti kanthu kalikonse kali ndi nthawi yake ndi chiweruzo chake; popeza zoipa za munthu zimchulukira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kanthu kalikonse kali ndi nthaŵi yake ndi kachitidwe kake, ngakhale kuti mavuto ake a munthu amamupsinja kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti pali nthawi yoyenera ndiponso machitidwe a chinthu chilichonse, ngakhale kuti mavuto ake a munthu amupsinja kwambiri. Onani mutuwo |