Mlaliki 8:5 - Buku Lopatulika5 Wosunga chilamulo sadzadziwa kanthu koipa; ndipo mtima wa munthu wanzeru udziwa nyengo ndi maweruzo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wosunga chilamulo sadzadziwa kanthu koipa; ndipo mtima wa munthu wanzeru udziwa nyengo ndi maweruzo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Womvera malamulo ake sadzaona vuto lililonse. Munthu wanzeru amadziŵa nthaŵi yake ndi njira yake yochitira zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aliyense amene amamvera lamulo lake sadzapeza vuto lililonse, ndipo munthu wanzeru amadziwa nthawi yoyenera ndi machitidwe ake. Onani mutuwo |