Mlaliki 7:9 - Buku Lopatulika9 Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Usamafulumira kukwiya, pakuti mkwiyo umakhalira zitsiru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Usamafulumire kukwiya mu mtima mwako, pakuti mkwiyo ndi bwenzi la zitsiru. Onani mutuwo |