Mlaliki 7:8 - Buku Lopatulika8 Chitsiriziro cha kanthu chiposa chiyambi chake; wofatsa mtima apambana wodzikuza mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chitsiriziro cha kanthu chiposa chiyambi chake; wofatsa mtima apambana wodzikuza mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake. Mtima wopirira ndi wopambana mtima wodzikuza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake, ndipo kufatsa nʼkwabwino kupambana kudzikuza. Onani mutuwo |