Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 7:10 - Buku Lopatulika

10 Usanene, Kodi bwanji masiku akale anapambana ano? Pakuti sulikufunsa mwanzeru pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Usanene, Kodi bwanji masiku akale anapambana ano? Pakuti sulikufunsa mwanzeru pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Usamafunsa kuti, “Chifukwa chiyani masiku amakedzana anali abwino kupambana masiku ano?” Limeneli si funso lanzeru.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Usamafunse kuti, “Nʼchifukwa chiyani masiku amakedzana anali abwino kupambana masiku ano?” pakuti si chinthu chanzeru kufunsa mafunso oterewa.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 7:10
9 Mawu Ofanana  

Nzeru ili yabwino pamodzi ndi cholowa; akuona dzuwa apindula nayo.


Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru.


Atero Yehova, Kalata ya chilekaniro cha amai ako ali kuti amene ndinamsudzula naye? Pena ndani wa angongole anga amene ndamgulitsa iwe? Taona chifukwa cha zoipa zanu munagulitsidwa, ndi chifukwa cha kulakwa kwanu amanu anachotsedwa.


Ndipo Gideoni ananena naye, Mbuye wanga, ngati Yehova ali nafe chatigwera ife bwanji chonsechi? Ndipo zili kuti zodabwitsa zake zonse zimene makolo athu anatiwerengera, ndi kuti, Sanatikweze kodi Yehova kuchokera mu Ejipito? Koma tsopano Yehova watitaya natipereka m'dzanja la Midiyani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa