Mlaliki 7:5 - Buku Lopatulika5 Kumva chidzudzulo cha anzeru kupambana kumva nyimbo ya zitsiru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Kumva chidzudzulo cha anzeru kupambana kumva nyimbo ya zitsiru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kuli bwino kuti munthu azimva kudzudzula kwa anthu anzeru, kupambana kumvera nyimbo zotamanda za zitsiru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kuli bwino kumva kudzudzula kwa munthu wanzeru kusiyana ndi kumvera mayamiko a zitsiru. Onani mutuwo |