Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 7:5 - Buku Lopatulika

5 Kumva chidzudzulo cha anzeru kupambana kumva nyimbo ya zitsiru.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Kumva chidzudzulo cha anzeru kupambana kumva nyimbo ya zitsiru.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Kuli bwino kuti munthu azimva kudzudzula kwa anthu anzeru, kupambana kumvera nyimbo zotamanda za zitsiru.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Kuli bwino kumva kudzudzula kwa munthu wanzeru kusiyana ndi kumvera mayamiko a zitsiru.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 7:5
14 Mawu Ofanana  

Akandipanda munthu wolungama ndidzati nchifundo: akandidzudzula, ndidzakuyesa mafuta a pamutu; mutu wanga usakane: Pakuti pangakhale posautsidwa iwo ndidzawapempherera.


Okhala pachipata akamba za ine; ndipo oledzera andiimba.


Wonyoza mau adziononga yekha; koma woopa malangizo adzalandira mphotho.


Wokana mwambo adzasauka nanyozedwa; koma wolabadira chidzudzulo adzalemekezedwa.


Chidzudzulo chilowa m'kati mwa wozindikira, kopambana ndi kukwapula wopusa kwambiri.


Monga mphete yagolide ndi chipini chagolide woyengeka, momwemo wanzeru wodzudzula pa khutu lomvera.


Kulasa kwa bwenzi kuli kokhulupirika; koma mdani apsompsona kawirikawiri.


Pakuti malangizo ndi nyali, malamulo ndi kuunika; ndi zidzudzulo za mwambo ndizo njira ya moyo.


Usadzudzule wonyoza kuti angakude; dzudzula wanzeru adzakukonda.


Mau a anzeru akunga zisonga, omwe akundika mau amene mbusa mmodzi awapatsa mau ao akunga misomali yokhomedwa zolimba.


Mtima wa anzeru uli m'nyumba ya maliro; koma mtima wa zitsiru uli m'nyumba ya kuseka.


Mau a anzeru achete amveka koposa kufuula kwa wolamulira mwa zitsiru.


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa