Mlaliki 7:18 - Buku Lopatulika18 Kuli kwabwino kugwira ichi; indetu, usachotsepo dzanja lako pakuti yemwe aopa Mulungu adzatuluka monsemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Kuli kwabwino kugwira ichi; indetu, usachotsepo dzanja lako pakuti yemwe aopa Mulungu adzatuluka monsemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nkwabwino kuti utsate njira imodzi, komanso osataya njira inayo. Munthu woopa Mulungu adzapeza phindu ndi ziŵiri zonsezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nʼkwabwino kuti utsate njira imodzi, ndipo usataye njira inayo. Munthu amene amaopa Mulungu adzapewa zinthu ziwiri zonsezi. Onani mutuwo |