Mlaliki 7:19 - Buku Lopatulika19 Nzeru ilimbitsa wanzeru koposa akulu khumi akulamulira m'mzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Nzeru ilimbitsa wanzeru koposa akulu khumi akulamulira m'mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Nzeru zimapatsa munthu mphamvu zoposa zimene angampatse atsogoleri khumi amumzinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Nzeru zimapereka mphamvu zambiri kwa munthu wanzeru kupambana olamulira khumi a mu mzinda. Onani mutuwo |