Mlaliki 7:17 - Buku Lopatulika17 Usapambanitse kuipa, ngakhale kupusa; uferenji nthawi yako isanafike? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Usapambanitse kuipa, ngakhale kupusa; uferenji nthawi yako isanafike? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Usachite kunyanyanso kuipa, usanyanye nawonso uchitsiru. Nanga uferenji nthaŵi yako isanakwane? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Usakhale woyipa kwambiri, ndipo usakhale chitsiru, uferenji nthawi yako isanakwane? Onani mutuwo |