Mlaliki 7:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti nzeru itchinjiriza monga ndalama zitchinjiriza; koma kudziwa kupambana, chifukwa nzeru isunga moyo wa eni ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti nzeru itchinjiriza monga ndalama zitchinjiriza; koma kudziwa kupambana, chifukwa nzeru isunga moyo wa eni ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chitetezo cha nzeru chili ngati chitetezo cha ndalama. Koma kudziŵa zinthu kukuposerapo, chifukwa nzeru zimasunga moyo wa amene ali nazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Nzeru ndi chitetezo, monganso ndalama zili chitetezo, koma phindu la chidziwitso ndi ili: kuti nzeru zimasunga moyo wa munthu amene ali nazo nzeruzo. Onani mutuwo |