Mlaliki 7:13 - Buku Lopatulika13 Tapenya ntchito ya Mulungu; pakuti ndani akhoza kulungamitsa chomwe iye anachikhotetsa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Tapenya ntchito ya Mulungu; pakuti ndani akhoza kulungamitsa chomwe iye anachikhotetsa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Taganizira ntchito ya Mulungu. Ndani angathe kuwongola chinthu chimene Iye adachipanga chokhota? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Taganizirani zimene Mulungu wazichita: ndani angathe kuwongola chinthu chimene Iye anachipanga chokhota? Onani mutuwo |