Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 5:5 - Buku Lopatulika

5 Kusawinda kupambana kuwinda osachita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Kusawinda kupambana kuwinda osachita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Kuli bwino kusalumbira kanthu kwa Mulungu, kupambana kuti ulumbire koma osachita.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Kuli bwino kusalumbira kusiyana ndi kulumbira koma osakwaniritsa lumbirolo.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 5:5
8 Mawu Ofanana  

Kunena mwansontho, Ichi nchopatulika, kuli msampha kwa munthu, ndi kusinkhasinkha pambuyo pake atawinda.


kapena munthu akalumbira ndi milomo yake osalingirira kuchita choipa, kapena kuchita chabwino, chilichonse munthu akalumbira osalingirira, ndipo chidambisikira; koma pochizindikira akhala wopalamula chimodzi cha izi:


Koma ine ndidzakupherani Inu nsembe ndi mau akuyamika, ndidzakwaniritsa chowinda changa. Chipulumutso ncha Yehova.


Pakuti milomo ya wansembe iyenera kusunga chidziwitso, ndi anthu ayenera kufunafuna chilamulo pakamwa pake; pakuti iye ndiye mthenga wa Yehova wa makamu.


Pamene unali nao, sunali wako kodi? Ndipo pamene unagulitsa sunali m'manja mwako kodi? Bwanji chinalowa ichi mumtima mwako? Sunanyenga anthu, komatu Mulungu.


Mukawindira Yehova Mulungu wanu chowinda, musamachedwa kuchichita; popeza Yehova Mulungu wanu adzakufunsani za ichi ndithu ndipo mukadachimwako.


Koma mukapanda kulonjeza chowinda, mulibe kuchimwa.


Ndipo kunali, pakumuona anang'amba zovala zake, nati, Tsoka ine, mwana wanga, wandiweramitsa kwakukulu, ndiwe wa iwo akundisaukitsa ine; pakuti ndamtsegulira Yehova pakamwa panga ine, ndipo sinditha kubwerera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa