Mlaliki 5:5 - Buku Lopatulika5 Kusawinda kupambana kuwinda osachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Kusawinda kupambana kuwinda osachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kuli bwino kusalumbira kanthu kwa Mulungu, kupambana kuti ulumbire koma osachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kuli bwino kusalumbira kusiyana ndi kulumbira koma osakwaniritsa lumbirolo. Onani mutuwo |