Mlaliki 5:4 - Buku Lopatulika4 Utawinda chiwindo kwa Mulungu, usachedwe kuchichita; pakuti sakondwera ndi zitsiru; chita chomwe unachiwindacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Utawinda chiwindo kwa Mulungu, usachedwe kuchichita; pakuti sakondwera ndi zitsiru; chita chomwe unachiwindacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ukalumbira chinthu kwa Mulungu, usachedwe kuchichita, chifukwa Mulungu sakondwera nazo zitsiru. Zimene wazilumbira, uzichitedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamene ulumbira kwa Mulungu usachedwe kukwaniritsa chimene walumbiracho. Iye sakondweretsedwa ndi chitsiru; kwaniritsa lumbiro lako. Onani mutuwo |