Mlaliki 5:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti loto lafika mwakuchuluka ntchito; ndipo mau a chitsiru mwakuchuluka maneno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti loto lafika mwakuchuluka ntchito; ndipo mau a chitsiru mwakuchuluka maneno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kuchuluka kwa mavuto mu mtima kumabweretsa maloto oipa, ndipo kuchuluka kwa mau kumadzetsa uchitsiru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kuchuluka kwa mavuto mu mtima kumabweretsa maloto oyipa, ndipo kuchuluka kwa mawu kumadzetsa uchitsiru. Onani mutuwo |