Mlaliki 5:12 - Buku Lopatulika12 Tulo ta munthu wogwira ntchito ntabwino, ngakhale adya pang'ono ngakhale zambiri; koma kukhuta kwa wolemera sikumgonetsa tulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Tulo ta munthu wogwira ntchito ntabwino, ngakhale adya pang'ono ngakhale zambiri; koma kukhuta kwa wolemera sikumgonetsa tulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Wantchito amagona tulo tabwino, ngakhale adye pang'ono kapena kudya kwambiri. Koma wolemera, chuma sichimgonetsa tulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Wantchito amagona tulo tabwino ngakhale adye pangʼono kapena kudya kwambiri, koma munthu wolemera, chuma sichimulola kuti agone. Onani mutuwo |